Top Latest News & Reports

...Boma la Mozambique Lapempha Mzika Zake Kuti Zibwelere Kwawo. Boma la Mozambique lapempha mzika zake zomwe zidathawa zipolowe zokhudza chisankho ndipo zikukhala m'dziko muno kuti zibwelere kwawo. Mtsogoleri wa Nthambi Yoona za Ngozi Zogwa Mwadzidzidzi…
Akuluakuluwa saadalekere pompo koma kukhotanso ku Kampu ya Nyamithuthu, yomwe ikusunga maanja pafupifupi 2,000 omwe adathawa zipolowe m’dziko la Mozambique. Uku anacheza ndi anthu akuluakulu komanso ana (omwe anawapeza akusewera mpira ndi masewero osiyanasiyana), kumva…
Motsogozedwa ndi Mkulu wa Nthambi Yoona za Ngozi Zogwa Mwadzidzidzi M’busa Charles Kalemba, akuluakulu ochokera ku ofesi za a Kazembe a maiko a Britain komanso United States kuno ku Malawi Lachinayi (pa 9 January, 2025)…

Visitors Counter